Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 20:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Inunso mukudziwa bwino kuti manja awa anagwira ntchito kuti ndipeze zosowa zanga+ ndi za amene ali nane.

  • 1 Akorinto 4:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 ndipo tikugwirabe ntchito yolimba+ ndi manja athu.+ Pamene akutinenera zachipongwe, timadalitsa.+ Pozunzidwa, timapirira.+

  • 1 Akorinto 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma sindinagwiritse ntchito dongosolo lililonse loterolo.+ Ndiponso, sikuti ndalemba zimenezi kuti dongosolo limeneli liyambe kugwira ntchito kwa ine ayi, pakuti zingakhale bwino kuti ineyo ndife kusiyana ndi kuti . . . ndipo palibe munthu angatsutse chifukwa chimene ndikudzitamira!+

  • 1 Atesalonika 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndithudi abale, mukukumbukira ntchito+ yathu imene tinagwira mwakhama ndi thukuta lathu. Mwa kugwira ntchito usiku ndi usana kuti aliyense wa inu asatilipirire kanthu kalikonse pofuna kutithandiza,+ tinalalikira uthenga wabwino wa Mulungu kwa inu.

  • 2 Atesalonika 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndiponso, pamene tinali ndi inu, tinali kukupatsani lamulo ili:+ “Ngati wina sakufuna kugwira ntchito, asadye.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena