Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Choncho Paulo anafika ku Debe ndiponso ku Lusitara.+ Kumeneko kunali wophunzira wina dzina lake Timoteyo,+ mwana wa mayi wachiyuda wokhulupirira, koma bambo ake anali Mgiriki.

  • 1 Atesalonika 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma Timoteyo wangofika kumene kwa ife kuchokera kwa inu+ ndipo watiuza nkhani yabwino ya kukhulupirika kwanu ndi chikondi+ chanu. Akuti mukupitiriza kutikumbukira nthawi zonse, ndiponso mukulakalaka kutiona, monganso mmene ife tikulakalakiradi kukuonani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena