Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 5:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakuti monga Atate amaukitsa akufa ndi kuwapatsa moyo,+ nayenso Mwana amapereka moyo kwa amene iye wafuna kuwapatsa.+

  • Yohane 6:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Pakuti chifuniro cha Atate wanga ndi chakuti, aliyense woona Mwana ndi kukhulupirira mwa iye akhale nawo moyo wosatha,+ ndipo ine ndidzamuukitsa pa tsiku lomaliza.”+

  • Chivumbulutso 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Kwa mngelo+ wa mpingo wa ku Simuna lemba kuti: Izi ndi zimene akunena ‘Woyamba ndi Wotsiriza,’+ amene anafa n’kukhalanso ndi moyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena