Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 4
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 4:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 18:5; Eze 20:11; Aro 10:5

Deuteronomo 4:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 12:32; Yos 1:7; Miy 30:6; Chv 22:18

Deuteronomo 4:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 25:3; Yos 22:17; Sl 106:28; Ho 9:10; 1Ak 10:7
  • +Nu 25:5, 9; 1Ak 10:8

Deuteronomo 4:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:20; 13:4; Yos 22:5

Deuteronomo 4:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 10:11; 26:46; Nu 30:16
  • +Le 25:18; Nu 36:13; De 6:1

Deuteronomo 4:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 2:3; Sl 19:7; 107:43; 111:10; 119:98; Miy 10:8; Yer 8:9
  • +Sl 119:100; Miy 4:7
  • +1Mf 4:34; 10:7; Da 1:20

Deuteronomo 4:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 7:23
  • +Eks 25:8; Le 26:12; De 5:26; Sl 46:1; 145:18

Deuteronomo 4:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 78:5; 147:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2002, ptsa. 14-15

    7/1/1992, ptsa. 11-12

Deuteronomo 4:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 4:23; 19:16
  • +Miy 4:21
  • +Miy 3:1; 7:1; Ahe 2:1
  • +Ge 18:19; De 6:7; Sl 78:5

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2006, ptsa. 29-30

    Sukulu ya Utumiki, tsa. 20

Deuteronomo 4:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:2
  • +Eks 19:9; Ahe 12:25
  • +Eks 20:20; De 5:29; 1Sa 12:24; Lu 1:50
  • +Miy 22:6; Aef 6:4

Deuteronomo 4:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:18; De 5:23; Ahe 12:18

Deuteronomo 4:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 9:10; 10:4
  • +De 4:15; Yes 40:18; Yoh 1:18; 4:24
  • +Eks 20:22; Ahe 12:19

Deuteronomo 4:13

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani mawu a m’munsi pa Eks 34:28.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:5; De 5:2; 9:9; Ahe 9:20
  • +Eks 20:1; 34:28; De 10:4
  • +Eks 24:12; 31:18; 32:19; 34:1

Deuteronomo 4:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 105:44

Deuteronomo 4:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 6:24; Yos 23:11
  • +De 4:12

Deuteronomo 4:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:7
  • +Eks 20:4; De 27:15; Yes 40:18; Mac 17:29; 1Ak 10:14

Deuteronomo 4:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 1:23
  • +De 5:8

Deuteronomo 4:18

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani mawu a m’munsi pa Eks 20:4.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 5:4

Deuteronomo 4:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 136:7; Yer 31:35
  • +De 17:3; 2Mf 17:16; Yer 8:2; Eze 8:16; Zef 1:5; Mac 7:43

Deuteronomo 4:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 8:51; Yer 11:4
  • +Eks 19:5; De 9:26; 1Mf 8:53; Sl 135:4

Deuteronomo 4:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 20:12; De 3:26
  • +De 31:2; Sl 106:32

Deuteronomo 4:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 3:27

Deuteronomo 4:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:5; 24:3
  • +Eks 20:4; De 4:16; 1Ak 10:14

Deuteronomo 4:24

Mawu a M'munsi

  • *

    Kapena kuti “iye ndi Mulungu wansanje (wachangu); Mulungu wosalola aliyense kupikisana naye.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 24:17; De 9:3; Ahe 12:29
  • +Eks 20:5; 34:14; Nu 25:11; Yos 24:19; Nah 1:2; Lu 10:27

Deuteronomo 4:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:7; De 4:16
  • +Owe 18:30; 2Mf 17:16; 21:7; Yes 42:8
  • +2Mf 17:17

Deuteronomo 4:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 30:19; 31:28; Yes 1:2
  • +Le 18:28; 26:32; De 29:28; Yos 23:16; Yes 24:1

Deuteronomo 4:27

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:64; Ne 1:8; Eze 12:15
  • +De 28:62

Deuteronomo 4:28

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 16:13; Eze 20:39
  • +De 28:36; Eze 20:32
  • +Sl 115:5; 135:16; Yes 44:9; Chv 9:20

Deuteronomo 4:29

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 30:10; 2Mb 15:4, 15
  • +De 30:2; 1Mf 8:48; Yer 29:13; Yow 2:12

Deuteronomo 4:30

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 30:10; 2Mb 33:13; Ne 1:9
  • +Yer 7:23

Deuteronomo 4:31

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:6; De 30:3; 2Mb 30:9; Ne 9:31; Sl 86:15; Yes 54:7; 55:7; 2Ak 1:3
  • +Le 26:42; Sl 105:8; Lu 1:72

Deuteronomo 4:32

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 44:1
  • +Ge 2:7
  • +Eks 15:11

Deuteronomo 4:33

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:26

Deuteronomo 4:34

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 7:19
  • +Eks 7:3
  • +Sl 105:27
  • +Eks 15:3
  • +Eks 13:3; De 6:21
  • +Eks 6:6
  • +De 26:8; Sl 78:49; Yer 32:21

Deuteronomo 4:35

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 3:14; 6:7; 1Mf 18:37; 2Mf 19:19; Sl 83:18
  • +Eks 15:11; De 32:39; 1Sa 2:2; Yes 45:18; Mko 12:32

Deuteronomo 4:36

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:18; 20:22; De 4:12, 15, 33; Ne 9:13; Ahe 12:18, 25

Deuteronomo 4:37

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:15; Sl 105:6
  • +Eks 13:14; Yer 32:21

Deuteronomo 4:38

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:28; De 7:1; 9:1; Yos 3:10; Sl 44:2

Deuteronomo 4:39

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 2:11; 2Mb 20:6; Sl 135:6; Da 4:35
  • +De 4:35; Yes 44:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 4

Deuteronomo 4:40

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:5
  • +De 5:16
  • +Ge 48:4

Deuteronomo 4:41

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 35:14

Deuteronomo 4:42

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 35:11, 22
  • +De 19:4
  • +Nu 35:25

Deuteronomo 4:43

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 21:36
  • +Yos 21:38
  • +Yos 21:27
  • +Yos 20:8

Deuteronomo 4:44

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 17:18; 27:3; Mki 4:4; Yoh 1:17; Aga 3:24

Deuteronomo 4:45

Mawu a M'munsi

  • *

    Kapena kuti “zikumbutso.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 6:17; 1Mf 2:3
  • +Le 26:46; De 4:1
  • +Le 18:5; De 4:5; Ne 9:13; Sl 119:164; Eze 20:11

Deuteronomo 4:46

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:5; 3:29
  • +Nu 21:26
  • +Nu 21:24

Deuteronomo 4:47

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 21:33; De 3:4; 29:7

Deuteronomo 4:48

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani mawu a m’munsi pa Ge 26:17.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 2:36; 3:12
  • +De 3:9; Yos 11:3

Deuteronomo 4:49

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:7; Yos 12:3
  • +Ge 14:3; De 3:17
  • +De 34:1

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 4:1Le 18:5; Eze 20:11; Aro 10:5
Deut. 4:2De 12:32; Yos 1:7; Miy 30:6; Chv 22:18
Deut. 4:3Nu 25:3; Yos 22:17; Sl 106:28; Ho 9:10; 1Ak 10:7
Deut. 4:3Nu 25:5, 9; 1Ak 10:8
Deut. 4:4De 10:20; 13:4; Yos 22:5
Deut. 4:5Le 10:11; 26:46; Nu 30:16
Deut. 4:5Le 25:18; Nu 36:13; De 6:1
Deut. 4:61Mf 2:3; Sl 19:7; 107:43; 111:10; 119:98; Miy 10:8; Yer 8:9
Deut. 4:6Sl 119:100; Miy 4:7
Deut. 4:61Mf 4:34; 10:7; Da 1:20
Deut. 4:72Sa 7:23
Deut. 4:7Eks 25:8; Le 26:12; De 5:26; Sl 46:1; 145:18
Deut. 4:8Sl 78:5; 147:19
Deut. 4:9Miy 4:23; 19:16
Deut. 4:9Miy 4:21
Deut. 4:9Miy 3:1; 7:1; Ahe 2:1
Deut. 4:9Ge 18:19; De 6:7; Sl 78:5
Deut. 4:10De 5:2
Deut. 4:10Eks 19:9; Ahe 12:25
Deut. 4:10Eks 20:20; De 5:29; 1Sa 12:24; Lu 1:50
Deut. 4:10Miy 22:6; Aef 6:4
Deut. 4:11Eks 19:18; De 5:23; Ahe 12:18
Deut. 4:12De 9:10; 10:4
Deut. 4:12De 4:15; Yes 40:18; Yoh 1:18; 4:24
Deut. 4:12Eks 20:22; Ahe 12:19
Deut. 4:13Eks 19:5; De 5:2; 9:9; Ahe 9:20
Deut. 4:13Eks 20:1; 34:28; De 10:4
Deut. 4:13Eks 24:12; 31:18; 32:19; 34:1
Deut. 4:14Sl 105:44
Deut. 4:15De 6:24; Yos 23:11
Deut. 4:15De 4:12
Deut. 4:16Eks 32:7
Deut. 4:16Eks 20:4; De 27:15; Yes 40:18; Mac 17:29; 1Ak 10:14
Deut. 4:17Aro 1:23
Deut. 4:17De 5:8
Deut. 4:181Sa 5:4
Deut. 4:19Sl 136:7; Yer 31:35
Deut. 4:19De 17:3; 2Mf 17:16; Yer 8:2; Eze 8:16; Zef 1:5; Mac 7:43
Deut. 4:201Mf 8:51; Yer 11:4
Deut. 4:20Eks 19:5; De 9:26; 1Mf 8:53; Sl 135:4
Deut. 4:21Nu 20:12; De 3:26
Deut. 4:21De 31:2; Sl 106:32
Deut. 4:22De 3:27
Deut. 4:23Eks 19:5; 24:3
Deut. 4:23Eks 20:4; De 4:16; 1Ak 10:14
Deut. 4:24Eks 24:17; De 9:3; Ahe 12:29
Deut. 4:24Eks 20:5; 34:14; Nu 25:11; Yos 24:19; Nah 1:2; Lu 10:27
Deut. 4:25Eks 32:7; De 4:16
Deut. 4:25Owe 18:30; 2Mf 17:16; 21:7; Yes 42:8
Deut. 4:252Mf 17:17
Deut. 4:26De 30:19; 31:28; Yes 1:2
Deut. 4:26Le 18:28; 26:32; De 29:28; Yos 23:16; Yes 24:1
Deut. 4:27De 28:64; Ne 1:8; Eze 12:15
Deut. 4:27De 28:62
Deut. 4:28Yer 16:13; Eze 20:39
Deut. 4:28De 28:36; Eze 20:32
Deut. 4:28Sl 115:5; 135:16; Yes 44:9; Chv 9:20
Deut. 4:29De 30:10; 2Mb 15:4, 15
Deut. 4:29De 30:2; 1Mf 8:48; Yer 29:13; Yow 2:12
Deut. 4:30De 30:10; 2Mb 33:13; Ne 1:9
Deut. 4:30Yer 7:23
Deut. 4:31Eks 34:6; De 30:3; 2Mb 30:9; Ne 9:31; Sl 86:15; Yes 54:7; 55:7; 2Ak 1:3
Deut. 4:31Le 26:42; Sl 105:8; Lu 1:72
Deut. 4:32Sl 44:1
Deut. 4:32Ge 2:7
Deut. 4:32Eks 15:11
Deut. 4:33De 5:26
Deut. 4:34De 7:19
Deut. 4:34Eks 7:3
Deut. 4:34Sl 105:27
Deut. 4:34Eks 15:3
Deut. 4:34Eks 13:3; De 6:21
Deut. 4:34Eks 6:6
Deut. 4:34De 26:8; Sl 78:49; Yer 32:21
Deut. 4:35Eks 3:14; 6:7; 1Mf 18:37; 2Mf 19:19; Sl 83:18
Deut. 4:35Eks 15:11; De 32:39; 1Sa 2:2; Yes 45:18; Mko 12:32
Deut. 4:36Eks 19:18; 20:22; De 4:12, 15, 33; Ne 9:13; Ahe 12:18, 25
Deut. 4:37De 10:15; Sl 105:6
Deut. 4:37Eks 13:14; Yer 32:21
Deut. 4:38Eks 23:28; De 7:1; 9:1; Yos 3:10; Sl 44:2
Deut. 4:39Yos 2:11; 2Mb 20:6; Sl 135:6; Da 4:35
Deut. 4:39De 4:35; Yes 44:6
Deut. 4:40De 4:5
Deut. 4:40De 5:16
Deut. 4:40Ge 48:4
Deut. 4:41Nu 35:14
Deut. 4:42Nu 35:11, 22
Deut. 4:42De 19:4
Deut. 4:42Nu 35:25
Deut. 4:43Yos 21:36
Deut. 4:43Yos 21:38
Deut. 4:43Yos 21:27
Deut. 4:43Yos 20:8
Deut. 4:44De 17:18; 27:3; Mki 4:4; Yoh 1:17; Aga 3:24
Deut. 4:45De 6:17; 1Mf 2:3
Deut. 4:45Le 26:46; De 4:1
Deut. 4:45Le 18:5; De 4:5; Ne 9:13; Sl 119:164; Eze 20:11
Deut. 4:46De 1:5; 3:29
Deut. 4:46Nu 21:26
Deut. 4:46Nu 21:24
Deut. 4:47Nu 21:33; De 3:4; 29:7
Deut. 4:48De 2:36; 3:12
Deut. 4:48De 3:9; Yos 11:3
Deut. 4:49De 1:7; Yos 12:3
Deut. 4:49Ge 14:3; De 3:17
Deut. 4:49De 34:1
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
  • 27
  • 28
  • 29
  • 30
  • 31
  • 32
  • 33
  • 34
  • 35
  • 36
  • 37
  • 38
  • 39
  • 40
  • 41
  • 42
  • 43
  • 44
  • 45
  • 46
  • 47
  • 48
  • 49
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 4:1-49

Deuteronomo

4 “Tsopano inu Aisiraeli, mverani malangizo ndi zigamulo zimene ndikukuphunzitsani kuti muzitsatira. Mukatero mudzakhala ndi moyo+ n’kukalowa m’dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu akukupatsani, ndi kukalitenga kukhala lanu. 2 Musawonjezepo kalikonse pa mawu amene ndikukulamulani, ndipo musachotsepo kalikonse pa mawu amenewa,+ kuti musunge malamulo a Yehova Mulungu wanu amene ndikukupatsani.

3 “Inu munaona ndi maso anu zimene Yehova anachita pa nkhani ya Baala wa ku Peori, kuti munthu aliyense amene anatsatira Baala wa ku Peori,+ Yehova Mulungu wanu anamuwononga ndi kum’chotsa pakati panu.+ 4 Koma nonsenu amene mukumamatira+ kwa Yehova Mulungu wanu muli ndi moyo lero. 5 Taonani, ndakuphunzitsani malangizo+ ndi zigamulo,+ monga mmene Yehova Mulungu wanga wandilamulira, kuti muzikatsatira zimenezo pamene mukukhala m’dziko limene mukupita kukalitenga kukhala lanu. 6 Ndipo muyenera kusunga malangizo ndi zigamulo zimenezi, chifukwa mukatero mudzakhala anzeru+ ndi ozindikira+ pamaso pa anthu a mitundu ina amene adzamva za malangizo onsewa. Pamenepo, anthuwo adzanena kuti, ‘Mtundu waukulu umenewu ndi wa anthu anzerudi ndi ozindikira.’+ 7 Pakuti ndi mtundu winanso uti wamphamvu+ umene milungu yake ili pafupi nawo, monga mmene Yehova Mulungu wathu alili pafupi ndi ife, tikamaitanira pa iye+ nthawi zonse? 8 Ndipo ndi mtundu winanso uti wamphamvu umene uli ndi malangizo ndi zigamulo zolungama zofanana ndi chilamulo chonsechi chimene ndikukuikirani pamaso panu lero?+

9 “Koma khalani tcheru ndipo musamale moyo wanu,+ kuti musaiwale zinthu zimene maso anu anaona,+ ndi kuti mitima yanu isaiwale zinthu zimenezo masiku onse a moyo wanu.+ Ana anu ndi zidzukulu zanu muziwauza za zinthu zimenezo,+ 10 za tsiku limene munaimirira pamaso pa Yehova Mulungu wanu ku Horebe,+ pamene Yehova anandiuza kuti, ‘Sonkhanitsa anthu kwa ine kuti amve mawu anga,+ naphunzire kundiopa+ masiku onse amene iwo adzakhala ndi moyo padziko, ndi kuti aphunzitsenso ana awo.’+

11 “Choncho anthu inu munayandikira ndi kuimirira m’munsi mwa phiri. Phiri limenelo linali kuyaka moto mpaka kumwamba, ndipo kunali mdima ndi mtambo wakuda.+ 12 Pamenepo Yehova anayamba kukulankhulani kuchokera pakati pa moto.+ Inu munamva mawu koma simunaone kalikonse.+ Munangomva mawu osaona kalikonse.+ 13 Pamenepo anakuuzani pangano lake,+ Mawu Khumi,*+ ndipo anakulamulani kuti muzilisunga. Kenako analemba Mawu Khumiwo pamiyala iwiri yosema.+ 14 Ndipo Yehova anandilamula pa nthawi imeneyo kuti ndikuphunzitseni malangizo ndi zigamulo, kuti muzikazitsatira pamene mukukhala m’dziko limene mukuwolokerako kukalitenga.+

15 “Chotero musamale moyo wanu,+ chifukwa pa tsiku limene Yehova analankhula nanu kuchokera pakati pa moto ku Horebe, simunaone kalikonse+ m’motomo. 16 Musamale kuti musachite zinthu zokuwonongetsani,+ kutinso musadzipangire chifaniziro, chifaniziro cha chinthu chilichonse, chachimuna kapena chachikazi,+ 17 chifaniziro cha nyama iliyonse ya padziko lapansi,+ chifaniziro cha mbalame iliyonse youluka m’mlengalenga,+ 18 chifaniziro cha chinthu chilichonse chimene chimayenda panthaka, ndi chifaniziro cha nsomba iliyonse+ ya m’madzi a pansi pa dziko.* 19 Musamale kuti musakweze maso anu kuthambo ndi kuona dzuwa, mwezi ndi nyenyezi, khamu lonse la zinthu zakuthambo, zimene Yehova Mulungu wanu wazipereka kwa anthu onse okhala pansi pa thambo lonse,+ n’kunyengeka nazo, kuzigwadira ndi kuyamba kuzitumikira.+ 20 Musachite zimenezo chifukwa Yehova ndiye anakutengani n’kukutulutsani m’ng’anjo yachitsulo,+ mu Iguputo, kuti mukhale anthu akeake+ monga mmene zilili lero.

21 “Ndipo Yehova anandikwiyira chifukwa cha inu,+ kotero kuti analumbira kuti ndisawoloke Yorodano, kapena kulowa m’dziko labwino limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kukhala cholowa chanu.+ 22 Ineyo ndifera m’dziko lino.+ Sindiwoloka Yorodano, koma inu muwoloka ndi kutenga dziko labwinoli. 23 Samalani kuti musaiwale pangano la Yehova Mulungu wanu limene anachita nanu,+ ndi kuti musadzipangire chifaniziro, chifaniziro cha chinthu chilichonse chimene Yehova Mulungu wanu anakuletsani.+ 24 Pakuti Yehova Mulungu wanu ndi moto wowononga,+ iye ndi Mulungu wofuna kuti anthu azidzipereka kwa iye yekha basi.*+

25 “Ukakakhala ndi ana ndi zidzukulu ndipo mwakhala nthawi yaitali m’dzikomo, n’kuchita zinthu zokuwonongetsa+ mwa kupanga chifaniziro,+ chifaniziro cha chinthu chilichonse, n’kuchita choipa pamaso pa Yehova Mulungu wako,+ moti n’kumulakwira, 26 ndikutenga kumwamba ndi dziko lapansi+ lero monga mboni zokutsutsani, kuti mudzafafanizidwa mwamsanga m’dziko limene mukupita kukalitenga mutawoloka Yorodano. Simudzatalikitsa masiku anu m’dzikomo chifukwa mudzawonongedwa ndithu.+ 27 Ndipo Yehova adzakubalalitsani pakati pa anthu a mitundu ina,+ ndipo mudzatsala ochepa+ m’mayiko a mitundu imene Yehova adzakuingitsiraniko. 28 Kumeneko mudzatumikira milungu+ yopangidwa ndi manja a anthu, milungu ya mtengo ndi mwala,+ imene siingaone, kumva, kudya kapena kununkhiza.+

29 “Mukadzafufuza Yehova Mulungu wanu muli kumeneko, mudzam’pezadi,+ chifukwa mudzam’funafuna ndi mtima wanu wonse ndiponso moyo wanu wonse.+ 30 Pamapeto pake, mawu amenewa akadzakwaniritsidwa pa inu, n’kukhala pamavuto aakulu, mudzabwereradi kwa Yehova Mulungu wanu+ ndi kumvetsera mawu ake.+ 31 Pakuti Yehova Mulungu wanu ndi Mulungu wachifundo.+ Sadzakutayani kapena kukuwonongani kapena kuiwala pangano+ la makolo anu limene anawalumbirira.

32 “Tafunsani tsopano, za masiku akale+ inu musanakhalepo, kuchokera pa tsiku limene Mulungu analenga munthu padziko lapansi,+ ndiponso kuchokera kumalekezero ena a thambo kukafika kumalekezero ena a thambo, Kodi chinthu chachikulu ngati chimenechi chinayamba chachitikapo, kapena kodi chinthu ngati chimenechi chinayamba chamvekapo?+ 33 Kodi anthu ena anamvapo mawu a Mulungu akumveka kuchokera pakati pa moto ngati mmene inuyo munawamvera, ndi kukhalabe ndi moyo?+ 34 Kapena kodi Mulungu anayamba wapitapo kukadzitengera mtundu wa anthu pakati pa mtundu wina ndi mayesero,+ zizindikiro,+ zozizwitsa,+ nkhondo,+ dzanja lamphamvu,+ mkono wotambasula,+ ndi zoopsa zazikulu+ zofanana ndi zimene Yehova Mulungu wanu anakuchitirani ku Iguputo inu mukuona? 35 Inuyo mwasonyezedwa zinthu zimenezi kuti mudziwe kuti Yehova ndiye Mulungu woona,+ ndipo palibenso wina.+ 36 Anakuchititsani kumva mawu ake kuchokera kumwamba n’cholinga chakuti akulangizeni kuti muzimumvera. Padziko lapansi pano, iye anakuchititsani kuona moto wake woopsa, ndipo munamva mawu ake kuchokera pakati pa moto.+

37 “Koma mukupitirizabe kukhala ndi moyo chifukwa anakonda makolo anu ndipo anasankha mbewu zawo zobwera pambuyo pawo,+ ndi kukutulutsani mu Iguputo ndi mphamvu zake zazikulu,+ komanso anali kukuyang’anirani. 38 Anachita izi kuti achotse mitundu yaikulu ndi yamphamvu kuposa inu, ndi kulowetsamo inu, kukupatsani dziko lawo kuti likhale cholowa chanu monga mmene zilili lero.+ 39 Inu mukudziwa bwino lero, ndipo muzikumbukira m’mitima yanu, kuti Yehova ndiye Mulungu woona, kumwamba ndiponso padziko lapansi.+ Palibenso wina.+ 40 Muzisunga malangizo+ ndi zigamulo zake zimene ndikukulamulani lero. Muzitero kuti nthawi zonse zinthu zikuyendereni bwino,+ inuyo ndi ana anu obwera pambuyo panu, ndiponso kuti mutalikitse masiku anu panthaka imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani.”+

41 Pa nthawi imeneyo, Mose anapatula mizinda itatu kuchigawo chotulukira dzuwa cha Yorodano,+ 42 kuti munthu wopha mnzake mwangozi,+ amene sanali kudana naye kale n’kale,+ azithawirako. Ameneyu azithawira ku umodzi mwa mizinda imeneyi ndi kukhala ndi moyo.+ 43 Mizinda yake ndi Bezeri,+ m’chipululu cha dera lokwererapo, wothawirako Arubeni, mzinda wa Ramoti+ ku Giliyadi, wothawirako Agadi, ndi mzinda wa Golani+ ku Basana, wothawirako Amanase.+

44 Tsopano chilamulo+ chimene Mose anaika pamaso pa ana a Isiraeli ndi ichi. 45 Chilamulocho ndicho maumboni,*+ malangizo+ ndi zigamulo+ zimene Mose anauza ana a Isiraeli pamene anatuluka mu Iguputo. 46 Anawauza zimenezi ali pafupi ndi Yorodano, m’chigwa, moyang’anizana ndi Beti-peori.+ Dera limeneli ndi dziko la Sihoni mfumu ya Aamori, imene inali kukhala ku Hesiboni.+ Mose ndi ana a Isiraeli anagonjetsa mfumuyi atatuluka mu Iguputo,+ 47 ndipo anamulanda dziko lakelo ndi dziko la Ogi+ mfumu ya Basana. Amenewa ndi mafumu awiri a Aamori amene anali kuchigawo chotulukira dzuwa cha Yorodano. 48 Dera limeneli linayambira ku Aroweli+ m’mphepete mwa chigwa* cha Arinoni mpaka kuphiri la Sione, limene ndi phiri la Herimoni,+ 49 ndiponso dera lonse la Araba+ m’chigawo cha kum’mawa kwa Yorodano, mpaka kunyanja ya Araba+ m’munsi mwa Pisiga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena