Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 10
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 10:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:1
  • +De 10:3

Deuteronomo 10:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:4

Deuteronomo 10:4

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani mawu a m’munsi pa Eks 34:28.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:15; 34:28
  • +Eks 20:1; De 4:13
  • +De 4:36; 5:4
  • +Eks 19:17; De 5:22

Deuteronomo 10:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:29
  • +De 10:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2006, tsa. 31

Deuteronomo 10:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 33:31
  • +Nu 20:23, 24; 33:38
  • +Nu 20:28

Deuteronomo 10:7

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani mawu a m’munsi pa Ge 26:17.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 33:33

Deuteronomo 10:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 1:50; 3:6; 8:14; 16:9
  • +Nu 3:31; 4:15; 1Mb 15:15
  • +De 18:5; 2Mb 29:11
  • +Nu 6:23; De 21:5; 2Mb 30:27

Deuteronomo 10:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 18:24; 26:62; De 18:1
  • +Nu 18:20

Deuteronomo 10:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 24:18; 34:28
  • +Eks 32:14
  • +Eze 33:11

Deuteronomo 10:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 15:18

Deuteronomo 10:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mik 6:8
  • +De 5:29; 6:13; Sl 34:9; Miy 8:13
  • +De 5:33; Yos 22:5; Eze 11:20
  • +De 30:16
  • +De 6:5; 11:13; Lu 10:27

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 25

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/2009, tsa. 10

Deuteronomo 10:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 24:7
  • +De 6:24

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/2009, tsa. 10

Deuteronomo 10:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 89:11; 115:16; Yes 66:1
  • +1Mb 29:11; Sl 24:1; 1Ak 10:26

Deuteronomo 10:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:37; Sl 105:6

Deuteronomo 10:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 30:6; Yer 4:4; Aro 2:29; Afi 3:3; Akl 2:11
  • +Eks 34:9; De 9:6; 31:27

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2007, tsa. 13

Deuteronomo 10:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 18:11; 2Mb 2:5; Sl 97:9
  • +Sl 136:3
  • +De 7:21; Ne 1:5; 9:32
  • +Yob 34:19; Mac 10:34; Aro 2:11; Aef 6:9
  • +2Mb 19:7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Yandikirani, tsa. 114

Deuteronomo 10:18

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu ake enieni, “mwana wamwamuna wopanda bambo.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 68:5; 146:9; Yak 1:27
  • +Le 19:10; De 24:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Yandikirani, ptsa. 113-114

Deuteronomo 10:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 19:34
  • +Eks 22:21

Deuteronomo 10:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 6:13
  • +Lu 4:8
  • +De 13:4
  • +De 6:13

Deuteronomo 10:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 15:2; Sl 105:45; Chv 19:6
  • +2Sa 7:23

Deuteronomo 10:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 46:27; Eks 1:5; Mac 7:14
  • +Ge 15:5; De 1:10; Ne 9:23

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 10:1Eks 34:1
Deut. 10:1De 10:3
Deut. 10:3Eks 34:4
Deut. 10:4Eks 32:15; 34:28
Deut. 10:4Eks 20:1; De 4:13
Deut. 10:4De 4:36; 5:4
Deut. 10:4Eks 19:17; De 5:22
Deut. 10:5Eks 34:29
Deut. 10:5De 10:2
Deut. 10:6Nu 33:31
Deut. 10:6Nu 20:23, 24; 33:38
Deut. 10:6Nu 20:28
Deut. 10:7Nu 33:33
Deut. 10:8Nu 1:50; 3:6; 8:14; 16:9
Deut. 10:8Nu 3:31; 4:15; 1Mb 15:15
Deut. 10:8De 18:5; 2Mb 29:11
Deut. 10:8Nu 6:23; De 21:5; 2Mb 30:27
Deut. 10:9Nu 18:24; 26:62; De 18:1
Deut. 10:9Nu 18:20
Deut. 10:10Eks 24:18; 34:28
Deut. 10:10Eks 32:14
Deut. 10:10Eze 33:11
Deut. 10:11Ge 15:18
Deut. 10:12Mik 6:8
Deut. 10:12De 5:29; 6:13; Sl 34:9; Miy 8:13
Deut. 10:12De 5:33; Yos 22:5; Eze 11:20
Deut. 10:12De 30:16
Deut. 10:12De 6:5; 11:13; Lu 10:27
Deut. 10:13Eks 24:7
Deut. 10:13De 6:24
Deut. 10:14Sl 89:11; 115:16; Yes 66:1
Deut. 10:141Mb 29:11; Sl 24:1; 1Ak 10:26
Deut. 10:15De 4:37; Sl 105:6
Deut. 10:16De 30:6; Yer 4:4; Aro 2:29; Afi 3:3; Akl 2:11
Deut. 10:16Eks 34:9; De 9:6; 31:27
Deut. 10:17Eks 18:11; 2Mb 2:5; Sl 97:9
Deut. 10:17Sl 136:3
Deut. 10:17De 7:21; Ne 1:5; 9:32
Deut. 10:17Yob 34:19; Mac 10:34; Aro 2:11; Aef 6:9
Deut. 10:172Mb 19:7
Deut. 10:18Sl 68:5; 146:9; Yak 1:27
Deut. 10:18Le 19:10; De 24:14
Deut. 10:19Le 19:34
Deut. 10:19Eks 22:21
Deut. 10:20De 6:13
Deut. 10:20Lu 4:8
Deut. 10:20De 13:4
Deut. 10:20De 6:13
Deut. 10:21Eks 15:2; Sl 105:45; Chv 19:6
Deut. 10:212Sa 7:23
Deut. 10:22Ge 46:27; Eks 1:5; Mac 7:14
Deut. 10:22Ge 15:5; De 1:10; Ne 9:23
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 10:1-22

Deuteronomo

10 “Pa nthawi imeneyo Yehova anandiuza kuti, ‘Dzisemere miyala iwiri yofanana ndi yoyamba ija,+ ndipo udzipangire likasa lamatabwa.+ Ukatero ukwere m’phiri muno kwa ine. 2 Pamiyalayo ndidzalembapo mawu amene anali pamiyala yoyamba ija, imene unaswa, ndipo udzaiike m’likasalo.’ 3 Choncho ndinapanga likasa la mtengo wa mthethe ndi kusema miyala iwiri yofanana ndi yoyamba ija.+ Kenako ndinakwera m’phiri, miyala iwiriyo ili m’manja mwanga. 4 Pamenepo analemba pamiyalayo mawu ofanana ndi oyamba aja,+ Mawu Khumi,*+ amene Yehova anakuuzani m’phiri kuchokera pakati pa moto,+ tsiku limene munasonkhana kuphiri.+ Atatero, Yehova anandipatsa miyalayo. 5 Ndiyeno ndinatembenuka, n’kutsika m’phirimo,+ ndipo ndinaika miyala iwiriyo m’likasa limene ndinapanga kuti izikhala mmenemo, monga mmene Yehova anandilamulira.+

6 “Pamenepo ana a Isiraeli ananyamuka kuchoka ku Beeroti Bene-yaakana+ kupita ku Mosera. Aroni anafera kumalo amenewo, ndipo anamuikanso kumeneko.+ Mwana wake Eleazara anayamba kutumikira monga wansembe m’malo mwa Aroniyo.+ 7 Ndiyeno ananyamuka pamalo amenewo kupita ku Gudigoda. Anachokanso ku Gudigoda kupita ku Yotibata,+ dziko la zigwa* zokhala ndi madzi ndithu.

8 “Pa nthawi imeneyo, Yehova anapatula fuko la Levi+ kuti lizinyamula likasa la pangano la Yehova,+ liziima pamaso pa Yehova pom’tumikira,+ ndi kuti lizidalitsa m’dzina lake kufikira lero.+ 9 N’chifukwa chake Levi alibe gawo ndiponso cholowa+ monga abale ake. Yehova ndiye cholowa chake, monga mmene Yehova Mulungu wanu anamuuzira.+ 10 Ndipo ine ndinakhala m’phirimo masiku ofanana ndi oyamba aja, masiku 40, usana ndi usiku,+ ndipo Yehova anandimveranso pa nthawi imeneyi.+ Yehova sanafune kukuwonongani.+ 11 Kenako Yehova anandiuza kuti, ‘Nyamuka, tsogolera anthu kuti ayambe ulendo, kuti akalowe ndi kutenga dziko limene ndinalumbirira makolo awo kuti ndidzawapatsa.’+

12 “Tsopano Aisiraeli inu, kodi Yehova Mulungu wanu akufuna kuti muzichita chiyani,+ koposa kuopa+ Yehova Mulungu wanu kuti muziyenda m’njira zake zonse,+ kukonda+ ndi kutumikira Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse, ndi moyo wanu wonse,+ 13 kuti muzisunga malamulo a Yehova ndi mfundo zake+ zimene ndikukupatsani lero, kuti zinthu zikuyendereni bwino?+ 14 Taonani, kumwamba ndi kwa Yehova Mulungu wanu,+ kumwambamwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi+ ndi zonse zili mmenemo ndi zake zonsezo. 15 Koma Yehova anadziphatika kwa makolo anu ndi kuwakonda, moti anasankha ana awo obadwa m’mbuyo mwawo,+ inuyo, pakati pa anthu onse monga mmene zilili lero. 16 Mitima yanu muichite mdulidwe+ ndipo musakhalenso ouma khosi.+ 17 Pakuti Yehova Mulungu wanu ndi Mulungu wa milungu+ ndi Mbuye wa ambuye.+ Iye ndi Mulungu wamkulu, wamphamvu ndi woopsa,+ amene sakondera+ munthu aliyense ndipo salandira chiphuphu.+ 18 Iye amaperekera chiweruzo ana amasiye* ndi akazi amasiye,+ ndipo amakonda mlendo wokhala pakati panu+ moti amam’patsa mkate ndi chofunda. 19 Inunso muzikonda mlendo wokhala pakati panu,+ chifukwa munali alendo m’dziko la Iguputo.+

20 “Muziopa Yehova Mulungu wanu.+ Muzim’tumikira,+ kum’mamatira+ ndi kulumbira pa dzina lake.+ 21 Iye ndi amene muyenera kum’tamanda,+ ndipo iye ndi Mulungu wanu amene wakuchitirani zinthu zazikulu ndi zochititsa mantha, zimene mwaziona ndi maso anu.+ 22 Makolo anu anapita ku Iguputo ndi anthu 70,+ ndipo tsopano Yehova Mulungu wanu wakuchulukitsani ngati nyenyezi zakuthambo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena