Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 7:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako Yehova anauza Nowa kuti: “Lowa mʼchingalawacho, iwe ndi banja lako, chifukwa iwe ndi amene ndakuona kuti ndiwe wolungama pakati pa mʼbadwo uwu.+

  • Ezekieli 14:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “‘Ngakhale amuna atatu awa: Nowa,+ Danieli+ ndi Yobu,+ akanakhala mʼdzikolo, iwo okhawo akanatha kupulumutsa miyoyo yawo chifukwa chokhala olungama,’+ akutero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”

  • Mateyu 24:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Chifukwa mofanana ndi mmene masiku a Nowa analili,+ ndi mmenenso kukhalapo* kwa Mwana wa munthu kudzakhalire.+

  • Aheberi 11:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Chifukwa cha chikhulupiriro, Nowa+ atachenjezedwa ndi Mulungu za zinthu zimene zinali zisanaoneke,+ anasonyeza kuopa Mulungu ndipo anamanga chingalawa+ kuti banja lake lipulumukiremo. Chifukwa cha chikhulupiriro, anatsutsa dziko+ ndipo anaonedwa kuti ndi wolungama chifukwa cha chikhulupirirocho.

  • 1 Petulo 3:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mizimuyi sinamvere Mulungu pa nthawi imene ankaleza mtima mʼmasiku a Nowa.+ Pa nthawiyo, Nowa ankapanga chingalawa+ chomwe chinapulumutsa pamadzi anthu owerengeka, anthu* 8 okha basi.+

  • 2 Petulo 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mulungu sanalekerere dziko lakale lija osalipatsa chilango,+ koma anasunga Nowa, yemwe ankalalikira za chilungamo cha Mulungu.+ Anamupulumutsa limodzi ndi anthu enanso 7,+ pamene anabweretsa chigumula padziko la anthu osaopa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena