Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 15:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma mʼbadwo wa 4 wa mbadwa zako ndi umene udzabwerere kuno,+ chifukwa nthawi yoti Aamori alangidwe sinakwane.”*+

  • Genesis 28:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ine ndili ndi iwe. Ndikuyangʼanira kulikonse kumene ungapite ndipo ndidzakubwezera kudziko lino.+ Sindidzakusiya mpaka nditachita zimene ndakulonjeza.”+

  • Genesis 47:29, 30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Tsopano nthawi yakuti Isiraeli amwalire inayandikira.+ Ndiye anaitana mwana wake Yosefe nʼkumuuza kuti: “Ngati ungandikomere mtima, ika dzanja lako pansi pa ntchafu yanga. Ulumbire kuti udzandisonyeza chikondi chokhulupirika komanso kuti udzakhala wokhulupirika kwa ine. Chonde, usadzandiike mʼmanda ku Iguputo kuno.+ 30 Ndikadzamwalira,* udzandinyamule kuchoka ku Iguputo kuno nʼkukandiika mʼmanda a makolo anga.”+ Yosefe anayankha kuti: “Ndidzachitadi mogwirizana ndi zimene mwanena.”

  • Genesis 50:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ana akewo anamunyamula nʼkupita naye kudziko la Kanani ndipo anakamuika mʼphanga mʼmunda wa Makipela, umene uli moyangʼanizana ndi munda wa Mamure. Mundawo ndi umene Abulahamu anagula kwa Efuroni, Muhiti, kuti akhale manda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena