Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 35:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mulungu anamuuza kuti: “Dzina lako ndi Yakobo.+ Kuyambira lero, dzina lako silikhalanso Yakobo, koma likhala Isiraeli.” Choncho anayamba kumutchula kuti Isiraeli.+ 11 Mulungu anamuuzanso kuti: “Ine ndine Mulungu Wamphamvuyonse.+ Ubereke ndipo ukhale ndi ana ambiri. Mitundu ndi mafuko ambiri adzatuluka mwa iwe,+ ndipo zina mwa mbadwa zako zidzakhala* mafumu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena