Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 20:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno Abimeleki anatenga nkhosa, ngʼombe ndiponso antchito aamuna ndi aakazi nʼkumupatsa Abulahamu. Anamubwezeranso Sara mkazi wake.

  • Genesis 24:34, 35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Iye anati: “Ine ndine mtumiki wa Abulahamu.+ 35 Yehova wamudalitsa kwambiri mbuye wanga ndipo wamupatsa chuma chambiri moti ali ndi nkhosa, ngʼombe, siliva, golide, antchito aamuna ndi aakazi komanso ngamila ndi abulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena