Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 17:29-31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Koma tsiku limene Loti anatuluka mu Sodomu, kumwamba kunagwa moto ndi sulufule ngati mvula nʼkuwononga anthu onse.+ 30 Zidzakhalanso chimodzimodzi pa tsikulo, pamene Mwana wa munthu adzaonekere.+

      31 Pa tsiku limenelo, munthu amene adzakhale padenga la nyumba koma katundu wake ali mʼnyumba, asadzatsike kukatenga katundu wakeyo. Chimodzimodzinso munthu amene adzakhale ali mʼmunda, asadzabwerere ku zinthu zimene wazisiya mʼmbuyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena