Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 17:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma za Isimaeli ndamva pempho lako. Iye ndidzamudalitsa ndipo ndidzamupatsa ana ambiri, komanso ndidzachulukitsa kwambiri mbadwa zake. Adzabereka ana 12 amene adzakhale atsogoleri a mafuko, ndipo ndidzamupangitsa kukhala mtundu waukulu.+

  • Genesis 37:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndiyeno abale akewo anakhala pansi kuti adye chakudya. Koma atayangʼana, anaona gulu la Aisimaeli+ amene ankachokera ku Giliyadi. Ngamila zawo zinali zitanyamula zinthu zonunkhira monga labidanamu, basamu komanso makungwa a utomoni wonunkhira.+ Iwo anali pa ulendo wopita ku Iguputo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena