3 Anakuphunzitsani kudzichepetsa pokulolani kuti mukhale ndi njala+ nʼkukudyetsani mana,+ amene inu kapena makolo anu sankawadziwa. Anachita zimenezi kuti mudziwe kuti munthu sangakhale ndi moyo ndi chakudya chokha, koma ndi mawu alionse ochokera mʼkamwa mwa Yehova.+