Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma ine ndidzalola Farao kuti aumitse mtima wake,+ ndipo ndidzachita zizindikiro ndi zodabwitsa zochuluka mʼdziko la Iguputo.+

  • Ekisodo 12:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndiyeno Aiguputo anayamba kuumiriza anthuwo kuti achoke mʼdzikolo mofulumira.+ Iwo anati, “chifukwa tonsefe tikungokhala ngati tafa kale!”+

  • Deuteronomo 6:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Choncho Yehova anapitiriza kuchita zizindikiro ndi zodabwitsa zazikulu ndiponso zowononga mu Iguputo monse,+ kwa Farao ndi kwa anthu onse amʼnyumba mwake, ife tikuona.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena