Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 38:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndipo siliva wa anthu amene anawerengedwa mʼgulu la Isiraeli, anali matalente 100 ndi masekeli 1,775 potengera muyezo wa sekeli lakumalo oyera.*

  • Numeri 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Uwerenge+ gulu lonse la Aisiraeli* mogwirizana ndi mabanja awo, potengera nyumba za makolo awo, nʼkulemba mayina awo. Uwerenge amuna onse, mmodzi ndi mmodzi.

  • 2 Samueli 24:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Davide atawerenga anthuwo, anayamba kuvutika mumtima mwake.*+ Choncho Davide anauza Yehova kuti: “Ndachimwa+ kwambiri pochita zimenezi. Chonde Yehova, ndikhululukireni tchimo langa ine mtumiki wanu,+ chifukwa ndachita zopusa kwambiri.”+

  • 2 Samueli 24:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako Yehova anagwetsa mliri+ mu Isiraeli kuyambira mʼmawa mpaka nthawi yomwe anakonza, moti anthu 70,000 anafa,+ kuyambira ku Dani mpaka ku Beere-seba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena