-
Levitiko 8:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Anawaza ena mwa mafuta odzozerawo maulendo 7 paguwa lansembe nʼkudzoza guwa lansembelo, zipangizo zake zonse, beseni ndi choikapo chake, kuti zikhale zopatulika.
-