Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 37:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Anapanganso mafuta ogwiritsa ntchito pa kudzoza kopatulika+ ndi mafuta onunkhira abwino kwambiri,+ osakanizidwa mwaluso.*

  • Salimo 141:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pemphero langa likhale ngati zofukiza+ zokonzedwa pamaso panu,+

      Mapembedzero anga akhale ngati nsembe yambewu yamadzulo.+

  • Chivumbulutso 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Atatenga mpukutuwo, angelo 4 ndi akulu 24 aja+ anagwada nʼkuwerama pamaso pa Mwanawankhosa. Aliyense wa iwo anali ndi zeze komanso mbale yagolide yodzaza ndi zofukiza. (Zofukizazo zikuimira mapemphero a oyera.)+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena