Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndiyeno pankhosayo utengepo mafuta ndi mchira wa mafuta ndi mafuta okuta matumbo, mafuta apachiwindi, impso ziwiri ndi mafuta ake+ ndi mwendo wakumbuyo wakumanja, chifukwa nkhosayo ndi yowaikira kuti akhale ansembe.+

  • Levitiko 9:18-20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno Aroni anapha ngʼombe yamphongo ndi nkhosa yamphongo ya nsembe yamgwirizano yoperekera anthuwo. Kenako ana ake anamupatsa magazi a nyamazo ndipo iye anawaza magaziwo mbali zonse za guwa lansembe.+ 19 Koma mafuta a ngʼombeyo,+ mchira wa mafuta wa nkhosa, mafuta okuta ziwalo za mʼmimba, impso ndi mafuta apachiwindi,+ 20 ana a Aroni anaika mafuta amenewo pamwamba pa zidale za nyamazo. Kenako anawotcha mafutawo paguwa lansembe.+

  • 2 Mbiri 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Solomo anapatula pakati pa bwalo la nyumba ya Yehova kuti aperekerepo nsembe zopsereza+ ndiponso mafuta a nsembe zamgwirizano. Anatero chifukwa paguwa lansembe lakopa*+ limene iye anamanga sipakanakwana kuperekerapo nsembe zopsereza,+ nsembe zambewu ndiponso mafuta.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena