Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Muzikumbukira tsiku la Sabata ndipo muziliona kuti ndi lopatulika.+

  • Ekisodo 20:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa kwa masiku 6 Yehova anapanga kumwamba, dziko lapansi, nyanja ndiponso zonse zimene zili mmenemo ndipo anayamba kupuma pa tsiku la 7.+ Nʼchifukwa chake Yehova anadalitsa tsiku la Sabata ndipo analipanga kukhala lopatulika.

  • Ekisodo 31:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Uuze Aisiraeli kuti, ‘Muonetsetse kuti mukusunga masiku anga a sabata.+ Chimenechi ndi chizindikiro pakati pa ine ndi inu mʼmibadwo yanu yonse, kuti mudziwe kuti ine Yehova ndakusankhani kukhala opatulika.

  • Luka 6:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kenako anapitiriza kuwauza kuti: “Mwana wa munthu ndi Mbuye wa Sabata.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena