Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Musapereke umboni wonamizira mnzanu.+

  • 1 Mafumu 21:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kenako amuna awiri opanda pake anabwera nʼkukhala kutsogolo kwa Naboti. Ndiyeno anayamba kupereka umboni wotsutsana ndi Naboti pamaso pa anthuwo. Iwo ananena kuti: “Naboti wanyoza Mulungu ndi mfumu!”+ Atatero anapita naye kunja kwa mzindawo nʼkukamuponya miyala mpaka kufa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena