Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 13:6-9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mchimwene wanu, amene ndi mwana wamwamuna wa mayi anu, kapena mwana wanu wamwamuna, mwana wanu wamkazi, mkazi wanu wokondedwa kapena mnzanu wapamtima, akayesa kukukopani mwachinsinsi pokuuzani kuti, ‘Tiyeni tikatumikire milungu ina,’+ milungu imene inuyo kapena makolo anu sankaidziwa, 7 kaya ndi milungu ya anthu amene akuzungulirani, amene akukhala pafupi ndi inu kapena amene akukhala kutali ndi inu, kuchokera kumalekezero ena a dziko kukafika kumalekezero ena, 8 musavomere kuchita zimene akufunazo kapena kumumvera.+ Musamumvere chisoni kapena kumuchitira chifundo kapenanso kumuteteza. 9 Koma muzimupha ndithu.+ Dzanja lanu lizikhala loyamba kumʼponya miyala kuti afe, ndipo anthu ena onse azibwera pambuyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena