Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Yehova anawonjezera kuti: “Ndaona mmene anthu anga amene ali ku Iguputo akuvutikira, ndipo ndamva kulira kwawo chifukwa cha amene akuwagwiritsa ntchito mwankhanza. Ndikudziwa bwino ululu umene akumva.+

  • Aefeso 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Inu ambuye, muzichitiranso akapolo anu chimodzimodzi. Musamawaopseze chifukwa mukudziwa kuti Ambuye wa nonsenu, wa iwowo ndi wa inuyo, ali kumwamba+ ndipo alibe tsankho.

  • Akolose 4:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Inu anthu amene ndinu ambuye, muzichitira akapolo anu zinthu zachilungamo ndi zoyenera, chifukwa mukudziwa kuti inunso muli ndi Ambuye kumwamba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena