Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 9:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Munthu adzacheka zimene zili kumbali yakumanja

      Koma adzakhalabe ndi njala.

      Ndipo munthu adzadya zimene zili kumanzere kwake

      Koma sadzakhuta.

      Aliyense adzadya mnofu wa dzanja lake,

  • Mika 6:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inu mudzadya, koma simudzakhuta.

      Ndipo mudzamvabe njala.+

      Mudzanyamula zinthu kuti mukazisunge pabwino, koma simudzatha kuziteteza.

      Zimene mudzatenge, ndidzazipereka kwa adani anu kuti aziwononge.

  • Hagai 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mwadzala mbewu zambiri, koma mukukolola zochepa.+ Mukudya, koma simukukhuta. Mukumwa koma simukukhutira. Mukuvala zovala, koma simukumva kutenthera. Ndipo amene akugwira ganyu akuika ndalama zake mʼmatumba obowoka.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena