Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 34:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mʼchaka cha 8 cha ulamuliro wake, akadali mnyamata, Yosiya anayamba kufunafuna Mulungu wa Davide kholo lake.+ Mʼchaka cha 12 anayamba kuyeretsa Yuda ndi Yerusalemu+ pochotsa malo okwezeka,+ mizati yopatulika,* zifaniziro zogoba+ ndiponso zifaniziro zachitsulo.

  • Yesaya 27:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Choncho mwa njira imeneyi zolakwa za Yakobo zidzaphimbidwa,+

      Ndipo tchimo lake likadzachotsedwa zotsatira zake zidzakhala izi:

      Adzasandutsa miyala yonse yapaguwa lansembe

      Kukhala ngati miyala yofewa kwambiri imene yanyenyekanyenyeka,

      Ndipo sipadzatsala mizati yopatulika* kapena maguwa ofukizirapo zonunkhira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena