-
2 Mafumu 17:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Iwo anapitiriza kukana malamulo ndi pangano+ limene iye anachita ndi makolo awo, ndiponso zikumbutso zimene iye anawapatsa powachenjeza.+ Mʼmalomwake ankatsatira mafano opanda pake+ ndipo nawonso anakhala opanda pake.+ Ankatengera mitundu yowazungulira imene Yehova anawalamula kuti asamaitsanzire.+
-