Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 12:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Uza Aisiraeli kuti, ‘Mkazi akakhala woyembekezera nʼkubereka mwana wamwamuna, azikhala wodetsedwa kwa masiku 7. Azikhala wodetsedwa ngati mmene amakhalira pa nthawi imene akusamba.+

  • Levitiko 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Wansembeyo aziona nthenda imene yatuluka pakhunguyo. Ngati cheya chapamalopo chasanduka choyera ndipo pakuoneka kuti nthendayo yalowa mpaka mkati mwa khungu, ndiye kuti limenelo ndi khate. Wansembe aziona nthendayo nʼkugamula kuti munthuyo ndi wodetsedwa.

  • Levitiko 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iye ndi wodetsedwa chifukwa cha zimene zikukhazo, kaya zinthuzo zikupitirizabe kutuluka kapena maliseche ake atsekeka ndi zimene zikukhazo, azikhalabe wodetsedwa.

  • Numeri 19:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Aliyense wokhudza mtembo wa munthu aliyense, azikhala wodetsedwa kwa masiku 7.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena