Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 3:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Uike Yoswa+ kuti akhale mtsogoleri ndipo umulimbikitse ndi kumulimbitsa mtima chifukwa ndi amene adzawolotse+ anthuwa ndi kuwachititsa kulandira dziko limene ulionelo kukhala cholowa chawo.’

  • Deuteronomo 31:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako Yehova anauza Mose kuti: “Taona, nthawi yoti ufe yayandikira.+ Itana Yoswa, ndipo mukaime pachihema chokumanako kuti ndikamuike kukhala mtsogoleri.”+ Choncho Mose ndi Yoswa anapita nʼkukaima pachihema chokumanako.

  • Deuteronomo 31:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndiyeno Mulungu anaika Yoswa+ mwana wa Nuni kuti akhale mtsogoleri, ndipo anamuuza kuti: “Limba mtima ndipo uchite zinthu mwamphamvu,+ chifukwa iwe ndi amene udzalowetse Aisiraeli mʼdziko limene ndawalumbirira,+ ndipo ine ndidzapitiriza kukhala ndi iwe.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena