Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 28:20-22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yakobo analonjeza kuti: “Mulungu akapitiriza kukhala nane komanso kunditeteza pa ulendo wangawu, ndiponso akadzandipatsa chakudya ndi zovala, 21 komanso ndikadzabwerera mwamtendere kunyumba ya bambo anga, pamenepo Yehova adzakhala atasonyezadi kuti ndi Mulungu wanga. 22 Mwala wachikumbutso umene ndauimika panowu, udzakhala nyumba ya Mulungu.+ Pa chilichonse chimene mudzandipatse, sindidzalephera kukubwezerani chakhumi.”

  • Oweruza 11:30, 31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndiyeno Yefita analonjeza+ Yehova kuti: “Mukapereka Aamoni mʼmanja mwanga, 31 aliyense amene adzatuluka mʼnyumba yanga kudzandichingamira pamene ndikubwera mwamtendere kuchokera kwa Aamoni, ndidzamʼpereka kwa inu Yehova+ kuti akhale nsembe yopsereza.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena