Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 30:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Zilipa kapolo wa Leya, anaberekera Yakobo mwana wamwamuna. 11 Zitatero Leya anati: “Ndachita mwayi!” Choncho anapatsa mwanayo dzina lakuti Gadi.*+

  • Genesis 46:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ana a Gadi+ anali Zifioni, Hagi, Suni, Eziboni, Eri, Arodi ndi Areli.+

  • Numeri 2:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako pazibwera fuko la Gadi. Mtsogoleri wa ana a Gadi ndi Eliyasafu,+ mwana wa Reueli. 15 Asilikali ake amene analembedwa mayina alipo 45,650.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena