Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 30:4-6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho Rakele anapereka kapolo wake Biliha kwa Yakobo kuti akhale mkazi wake, ndipo iye anagona naye.+ 5 Biliha anakhala woyembekezera ndipo patapita nthawi anamuberekera Yakobo mwana wamwamuna. 6 Ndiyeno Rakele anati: “Mulungu wakhala woweruza wanga komanso wamva mawu anga, ndipo wandipatsa mwana wamwamuna.” Nʼchifukwa chake Rakele anapatsa mwanayo dzina lakuti Dani.*+

  • Genesis 46:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mwana wa* Dani+ anali Husimu.+

  • Numeri 2:25, 26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Amene azimanga msasa wawo kumpoto ndi gulu la mafuko atatu la Dani ndi magulu awo.* Mtsogoleri wa ana a Dani ndi Ahiyezeri,+ mwana wa Amisadai. 26 Asilikali ake amene analembedwa mayina alipo 62,700.+

  • Numeri 10:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pomaliza, gulu la mafuko atatu la ana a Dani linanyamuka potengera magulu awo.* Iwo ndi amene ankalondera kumbuyo kwa magulu onse a mafukowo. Mtsogoleri wa gululi anali Ahiyezeri,+ mwana wa Amisadai.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena