Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 30:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Biliha kapolo wa Rakele anakhalanso woyembekezera moti patapita nthawi anamuberekera Yakobo mwana wina wamwamuna. 8 Ndiyeno Rakele anati: “Ndalimbana mwamphamvu ndi mchemwali wanga ndipo ndapambananso.” Choncho anapatsa mwanayo dzina lakuti Nafitali.*+

  • Genesis 46:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ana a Nafitali+ anali Yahazeeli, Guni, Yezera ndi Silemu.+

  • Numeri 2:29, 30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kenako pazibwera fuko la Nafitali. Mtsogoleri wa ana a Nafitali ndi Ahira,+ mwana wa Enani. 30 Asilikali ake amene analembedwa mayina alipo 53,400.+

  • Numeri 26:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Ana aamuna a Nafitali+ potengera mabanja awo anali awa: Yahazeeli amene anali kholo la banja la Ayahazeeli, Guni amene anali kholo la banja la Aguni,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena