Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 36:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho Esau anakakhazikika kudera lamapiri ku Seiri.+ Dzina lina la Esau linali Edomu.+

  • Deuteronomo 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Auze anthuwo kuti: “Mudutsa mʼmalire a dziko la abale anu, mbadwa za Esau,+ amene akukhala ku Seiri.+ Iwo adzachita nanu mantha,+ choncho muyenera kukhala osamala kwambiri.

  • Deuteronomo 23:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Musamadane ndi mbadwa ya Edomu, chifukwa ndi mʼbale wanu.+

      Musamadane ndi munthu wa ku Iguputo, chifukwa munali alendo mʼdziko lawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena