Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 20:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Choncho mfumu ya Edomu inakana kulola Aisiraeli kudzera mʼdziko lake. Zitatero, Aisiraeli analambalala dziko la Edomu.+

  • Deuteronomo 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho tinadutsa pafupi ndi abale athu, mbadwa za Esau,+ amene akukhala ku Seiri, ndipo sitinayende njira ya Araba, Elati ndi Ezioni-geberi.+

      Kenako tinatembenuka nʼkudutsa njira ya mʼchipululu cha Mowabu.+

  • Oweruza 11:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamene ankadutsa mʼchipululu, analambalala dziko la Edomu+ ndi la Mowabu. Anadutsa chakumʼmawa kwa dziko la Mowabu+ nʼkukamanga misasa mʼchigawo cha Arinoni. Iwo sanadutse malire a Mowabu chifukwa Arinoni ndi amene anali malire a Mowabu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena