Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mʼchaka chachitatu cha Hoshiya+ mwana wa Ela mfumu ya Isiraeli, Hezekiya+ mwana wa Ahazi,+ mfumu ya Yuda anakhala mfumu.

  • 2 Mafumu 18:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Hezekiya ndi amene anachotsa malo okwezeka,+ kugwetsa zipilala zopatulika ndiponso kudula mzati wopatulika.*+ Komanso iye anaphwanyaphwanya njoka yakopa* imene Mose anapanga,+ chifukwa pa nthawiyi Aisiraeli ankafukiza nsembe yautsi kwa njokayo ndipo inkatchedwa fano la njoka yakopa.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena