Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 3:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Kwera pamwamba pa Pisiga+ ndipo ukayangʼane kumadzulo, kumpoto, kumʼmwera ndi kumʼmawa kuti ukaone dzikolo ndi maso ako, chifukwa suwoloka Yorodano uyu.+

  • Deuteronomo 34:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Kenako Mose anachoka mʼchipululu cha Mowabu kupita mʼphiri la Nebo,+ pamwamba pa Pisiga,+ moyangʼanizana ndi Yeriko.+ Ndipo Yehova anamuonetsa dziko lonse, kuchokera ku Giliyadi mpaka ku Dani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena