Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 38:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kumeneko Yuda anaona mwana wamkazi wa munthu wina wa Chikanani+ ndipo anamukwatira. Munthuyo dzina lake anali Sua.

  • Genesis 38:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Anaberekanso mwana wina wamwamuna nʼkumupatsa dzina lakuti Shela. Pa nthawi imene mwanayu ankabadwa, Yuda anali ku Akizibu.+

  • Genesis 38:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndiyeno Yuda atayangʼanitsitsa zinthuzo, ananena kuti: “Mkaziyu ndi wolungama koposa ine, chifukwa sindinamupereke kwa mwana wanga Shela.”+ Zitatero, Yuda sanagonenso naye.

  • 1 Mbiri 4:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ana a Shela+ mwana wa Yuda anali Ere bambo a Leka, Laada bambo a Maresha, mabanja a Asibeya omwe ankagwira ntchito yopanga nsalu zabwino kwambiri,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena