12 “Ine ndi amene ndinanena zimene zidzachitike, amene ndinakupulumutsani komanso amene ndinachititsa kuti zimenezi zidziwike,
Pa nthawi imene pakati panu panalibe mulungu wachilendo.+
Choncho inuyo ndinu mboni zanga, ndipo ine ndine Mulungu,” akutero Yehova.+