Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho analirira Yehova kuti awathandize+ ndipo anati, ‘Tachimwa,+ chifukwa tasiya Yehova nʼkuyamba kutumikira Abaala+ ndi zifaniziro za Asitoreti.+ Tsopano tipulumutseni kwa adani athu kuti tizikutumikirani.’

  • 1 Samueli 12:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Musapatuke nʼkuyamba kutsatira milungu yopanda pake*+ yomwe ndi yosathandiza+ komanso singakupulumutseni chifukwa ndi yopanda pake.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena