Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mʼdziko lanu simudzapezeka mkazi wopititsa padera kapena wosabereka.+ Ndipo ndidzachulukitsa masiku a moyo wanu.*

  • Deuteronomo 28:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova adzakupatsani ana ambiri komanso ziweto zochuluka ndipo nthaka+ yamʼdziko limene Yehova analumbira kwa makolo anu kuti adzakupatsani, idzabereka zipatso zambiri.+

  • Salimo 127:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Taonani! Ana ndi cholowa chochokera kwa Yehova.+

      Chipatso cha mimba ndi mphoto yochokera kwa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena