Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 6:23-27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Uza Aroni ndi ana ake kuti, ‘Mukamadalitsa+ Aisiraeli muziwauza kuti:

      24 “Yehova akudalitseni+ ndipo akutetezeni.

      25 Yehova asonyeze kuti akusangalala nanu+ ndipo akukomereni mtima.

      26 Yehova akuyangʼaneni mokondwera ndipo akupatseni mtendere.”’+

      27 Aroni ndi ana ake azigwiritsa ntchito dzina langa podalitsa Aisiraeli+ kuti ine ndiwadalitse.”+

  • Deuteronomo 21:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ansembe, omwe ndi Alevi, azifika pafupi chifukwa ndi amene Yehova Mulungu wanu wawasankha kuti azimutumikira+ komanso azidalitsa mʼdzina la Yehova.+ Iwo ndi amene akuyenera kunena njira yothetsera mkangano uliwonse wokhudza zinthu zankhanza zimene zachitika.+

  • 2 Mbiri 30:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pomaliza, Alevi omwe anali ansembe anaimirira nʼkudalitsa anthuwo.+ Mulungu anamva mawu awo ndipo pemphero lawo linafika kumwamba, kumalo oyera omwe iye amakhala.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena