9 Kenako iye anati: “Tsopano ngati mwandikomera mtima, inu Yehova, chonde Yehova, muyende nafe ndipo mukhale pakati pathu,+ ngakhale kuti ndife anthu ouma khosi.+ Mutikhululukirenso zolakwa zathu ndi machimo athu,+ ndipo mutitenge kukhala chuma chanu.”