Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 34:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kenako iye anati: “Tsopano ngati mwandikomera mtima, inu Yehova, chonde Yehova, muyende nafe ndipo mukhale pakati pathu,+ ngakhale kuti ndife anthu ouma khosi.+ Mutikhululukirenso zolakwa zathu ndi machimo athu,+ ndipo mutitenge kukhala chuma chanu.”

  • Deuteronomo 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho mudziwe kuti Yehova Mulungu wanu sakukupatsani dziko labwinoli chifukwa choti ndinu olungama, paja ndinu anthu ouma khosi.+

  • Deuteronomo 31:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ineyo ndikudziwa bwino khalidwe lanu lopanduka+ ndi kuuma mtima* kwanu.+ Ngati mwakhala mukupandukira Yehova pamene ndili moyo, ndiye kuli bwanji pambuyo pa imfa yanga!

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena