Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 12:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Simudzaloledwa kudyera mʼmizinda yanu* chakhumi cha mbewu zanu, vinyo wanu watsopano, mafuta anu, ana oyamba kubadwa a ngʼombe zanu ndi a nkhosa zanu,+ iliyonse mwa nsembe zimene mukupereka pokwaniritsa lonjezo limene mwachita, nsembe zanu zaufulu kapena chopereka chochokera mʼmanja mwanu.

  • Deuteronomo 15:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mwana aliyense wamphongo woyamba kubadwa wa ngʼombe kapena wa nkhosa muzimupatula nʼkumupereka kwa Yehova Mulungu wanu.+ Musamagwiritse ntchito iliyonse mwana woyamba kubadwa wa ngʼombe,* kapena kumeta ubweya wa mwana woyamba kubadwa wa nkhosa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena