Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 21:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Aliyense amene amatseka khutu lake kuti asamve kudandaula kwa munthu wonyozeka,

      Nayenso adzaitana koma sadzayankhidwa.+

  • Yakobo 2:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ngati mʼbale kapena mlongo alibe zovala* komanso chakudya chokwanira pa tsikulo, 16 koma wina mwa inu nʼkumuuza kuti, “Uyende bwino, upeze zovala ndi zakudya za tsiku lililonse,” koma osamupatsa zimene akufunikirazo kuti akhale ndi moyo, kodi pali phindu lanji?+

  • 1 Yohane 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Aliyense amene ali ndi zinthu zofunika pa moyo ndipo akuona mʼbale wake akuvutika chifukwa chosowa zinthuzo, koma osamusonyeza chifundo, kodi tingati munthu ameneyu amakonda Mulungu?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena