Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 29:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 ‘Pamene ndinkakutsogolerani kwa zaka 40 mʼchipululu,+ zovala zanu sizinathe ndiponso nsapato zanu sizinathe kumapazi anu.+

  • Nehemiya 9:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kwa zaka 40 munawapatsa chakudya mʼchipululu+ moti sanasowe kanthu. Zovala zawo sizinathe+ ndipo mapazi awo sanatupe.

  • Salimo 23:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yehova ndi Mʼbusa wanga.+

      Sindidzasowa kanthu.+

  • Salimo 34:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Opani Yehova, inu oyera ake onse,

      Chifukwa onse amene amamuopa sasowa kanthu.+

      כ [Kaph]

      10 Ngakhale mikango yamphamvu* ingakhale ndi njala chifukwa chosowa chakudya.

      Koma anthu amene akufunafuna Yehova sadzasowa chilichonse chabwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena