39 Koma Isaki bambo ake anamuuza kuti:
“Taona, udzakhala kutali ndi nthaka yachonde, komanso kutali ndi mame akumwamba.+ 40 Pa nthawi yonse ya moyo wako uzidzadalira lupanga+ ndipo udzatumikira mʼbale wako.+ Koma ukadzatopa ndi goli lake, udzalithyola ndi kulichotsa mʼkhosi mwako.”+