-
Ezekieli 18:28Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
28 Munthu woipayo akazindikira kuti zimene akuchita ndi zoipa nʼkusiya kuchita zoipazo, ndithu iye adzapitiriza kukhala ndi moyo. Sadzafa ayi.
-