Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Oyamba kubwerera nʼkukakhala kucholowa chawo mʼmizinda yawo anali Aisiraeli ena, ansembe, Alevi ndi atumiki apakachisi.*+

  • Ezara 7:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndikufuna kukuuzaninso kuti si zololeka kulandira msonkho kuchokera kwa ansembe, Alevi, oimba,+ alonda apakhomo, atumiki a pakachisi*+ ndi anthu ogwira ntchito panyumba ya Mulungu. Musawakhometse msonkho umene munthu aliyense amakhoma, msonkho wakatundu+ komanso msonkho wamsewu.

  • Ezara 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako ndinawalamula kuti apite kwa Ido yemwe anali mtsogoleri pamalo otchedwa Kasifiya. Ndinawauza mawu oti akauze Ido ndi abale ake, atumiki apakachisi* omwe anali ku Kasifiyako kuti atibweretsere atumiki apanyumba ya Mulungu wathu.

  • Nehemiya 3:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Atumiki apakachisi*+ omwe ankakhala ku Ofeli+ anakonza mpandawo mpaka patsogolo pa Geti la Kumadzi,+ kumʼmawa. Iwo anakonzanso nsanja yomwe inatulukira kunja kwa mpanda.

  • Nehemiya 7:60
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 60 Atumiki apakachisi*+ onse ndiponso ana a atumiki a Solomo analipo 392.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena