Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 33:13-15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ponena za Yosefe anati:+

      “Dziko lake lidalitsidwe ndi Yehova.+

      Lidalitsidwe ndi zinthu zabwino kwambiri zakumwamba,

      Ndi mame komanso madzi ochokera mu akasupe a pansi pa nthaka.+

      14 Lidalitsidwenso ndi zinthu zabwino kwambiri, zochokera ku dzuwa,

      Ndi zokolola zabwino kwambiri mwezi uliwonse,+

      15 Lidalitsidwe ndi zinthu zabwino koposa zamʼmapiri akale,*+

      Ndi zinthu zabwino kwambiri zamʼmapiri amene adzakhalapo mpaka kalekale.

  • Yoswa 17:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Poyankha, Yoswa anauza anthu a fuko la Yosefe, omwe ndi ana a Efuraimu ndi Manase, kuti: “Ndinu ambiri ndipo ndinu amphamvu kwambiri. Simuyenera kukhala ndi gawo limodzi lokha,+ 18 koma mutengenso dera lamapiri.+ Ngakhale kuti ndi lankhalango, mudzagwetsamo mitengo ndipo gawo lanu likathera kumeneko. Mudzathamangitsa Akanani ngakhale kuti ndi amphamvu ndipo ali ndi magaleta ankhondo okhala ndi zitsulo zazitali zakuthwa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena