Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pamene Samueli ankapereka nsembe yopsereza, Afilisiti anali akuyandikira kuti amenyane ndi Isiraeli. Zitatero, Yehova anachititsa mabingu amphamvu kwambiri+ pa tsiku limenelo kuti asokoneze+ Afilisiti. Choncho Afilisitiwo anagonjetsedwa ndi Aisiraeli.+

  • 2 Samueli 22:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako Yehova ali kumwamba anayamba kugunda ngati mabingu;+

      Wamʼmwambamwamba anachititsa kuti mawu ake amveke.+

  • Salimo 18:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kenako Yehova anayamba kugunda ngati mabingu ali kumwamba.+

      Wamʼmwambamwamba anachititsa kuti mawu ake amveke,+

      Ndipo kunagwa matalala ndi makala a moto.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena