Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iye adzawauza kuti: “Inetu ndasankha mfumu yanga+

      Ndipo ikulamulira ku Ziyoni,+ phiri langa lopatulika.”

  • Salimo 110:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 110 Yehova anauza Ambuye wanga kuti:

      “Khala kudzanja langa lamanja+

      Mpaka nditaika adani ako kuti akhale chopondapo mapazi ako.”+

  • Mateyu 28:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Tsopano Yesu anayandikira nʼkuwauza kuti: “Ulamuliro wonse waperekedwa kwa ine kumwamba ndi padziko lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena