Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 17:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Davide anayamba kufunsa asilikali amene anali naye pafupi kuti: “Kodi munthu amene angaphe Mfilisitiyu nʼkuchititsa kuti Aisiraeli asiye kunyozedwa amupatsa chiyani? Kodi Mfilisiti wosadulidwa ameneyu ndi ndani kuti azinyoza asilikali a Mulungu wamoyo?”+

  • 1 Samueli 17:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ine mtumiki wanu ndinapha zilombo ziwiri zonsezi, mkango komanso chimbalangondo. Mfilisiti wosadulidwayu akhalanso ngati chimodzi mwa zilombo zimenezi, chifukwa wanyoza asilikali a Mulungu wamoyo.”+

  • 2 Samueli 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako Davide anatumiza uthenga kwa Isi-boseti+ mwana wa Sauli wakuti: “Ndipatse mkazi wanga Mikala, amene ndinamuperekera malowolo a makungu okwana 100 a Afilisiti, amene amachotsa pochita mdulidwe.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena